1 Akorinto 10:17 - Buku Lopatulika17 Pakuti mkate ndiwo umodzi, chotero ife ambiri ndife thupi limodzi; pakuti ife tonse titengako kumkate umodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Pakuti mkate ndiwo umodzi, chotero ife ambiri ndife thupi limodzi; pakuti ife tonse titengako kumkate umodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Popeza kuti mkate ndi umodzi wokha, ife tonse, ngakhale tili ambiri, ndife thupi limodzi, chifukwa tonse timagaŵana mkate umodzi womwewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Pakuti buledi ndi mmodzi yekha, ifenso ngakhale tili ambiri, ndife thupi limodzi, popeza tonse timagawana buledi mmodzi yemweyo. Onani mutuwo |