1 Akorinto 1:15 - Buku Lopatulika15 kuti anganene mmodzi kuti mwabatizidwa m'dzina langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 kuti anganene mmodzi kuti mwabatizidwa m'dzina langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Motero palibe amene anganene kuti adabatizidwa m'dzina langa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 mwakuti palibe amene anganene kuti anabatizidwa mʼdzina langa. Onani mutuwo |