1 Akorinto 1:12 - Buku Lopatulika12 Koma ichi ndinena, kuti yense wa inu anena, Ine ndine wa Paulo; koma ine wa Apolo; koma ine wa Kefa; koma ine wa Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Koma ichi ndinena, kuti yense wa inu anena, Ine ndine wa Paulo; koma ine wa Apolo; koma ine wa Kefa; koma ine wa Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Chimene ndikufuna kunena nchakuti aliyense mwa inu akungonena zakezake. Wina akuti, “Ine ndine wa Paulo,” winanso akuti, “Ine ndine wa Apolo,” wina akuti, “Ine ndine wa Kefa,” winanso akuti, “Ine ndine wa Khristu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Chimene ndikutanthauza ndi ichi: wina amati, “Ndimatsatira Paulo,” wina, “Ndimatsatira Apolo,” wina, “Ndimatsatira Kefa,” winanso, “Ndimatsatira Khristu.” Onani mutuwo |