1 Akorinto 1:11 - Buku Lopatulika11 Pakuti zinamveka kwa ine za inu, abale anga, ndi iwo a kwa Koloe, kuti pali makani pakati pa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pakuti zinamveka kwa ine za inu, abale anga, ndi iwo a kwa Koloe, kuti pali makani pakati pa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Pakuti ena a m'banja la Koloe andifotokozera kuti pali kukangana pakati panu, abale anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Abale anga, ena a ku nyumba ya Kloe andidziwitsa kuti pali mkangano pakati panu. Onani mutuwo |