Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 7:2 - Buku Lopatulika

Koma chikondwerero cha Ayuda cha Misasa, linayandikira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma chikondwerero cha Ayuda cha Misasa, linayandikira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthaŵiyo nkuti chikondwerero cha Misasa chili pafupi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma phwando la Ayuda lamisasa litayandikira,

Onani mutuwo



Yohane 7:2
10 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu onse a Israele anasonkhana kwa mfumu Solomoni kukadyerera m'mwezi wa Etanimu, ndiwo mwezi wachisanu ndi chiwiri.


Ndipo nthawi yomweyo Solomoni anachita madyerero pamaso pa Yehova Mulungu wathu, ndi Israele yense pamodzi naye, msonkhano waukulu wakuyambira polowera ku Hamati kufikira ku nyanja ya ku Ejipito, masiku asanu ndi awiri, ndi masiku asanu ndi awiri ena, ndiwo masiku khumi mphambu anai.


Nachita chikondwerero cha Misasa monga kwalembedwa, napereka nsembe yopsereza tsiku ndi tsiku mawerengedwe ake, monga mwa lamulo lake la tsiku lake pa tsiku lake;