1 Mafumu 8:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anthu onse a Israele anasonkhana kwa mfumu Solomoni kukadyerera m'mwezi wa Etanimu, ndiwo mwezi wachisanu ndi chiwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anthu onse a Israele anasonkhana kwa mfumu Solomoni kukadyerera m'mwezi wa Etanimu, ndiwo mwezi wachisanu ndi chiwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndipo Aisraele onse adasonkhana pamaso pa mfumu Solomoni nthaŵi ya chikondwerero cha mwezi wa Etanimu, mwezi wachisanu ndi chiŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Aisraeli onse anasonkhana pamaso pa Mfumu Solomoni nthawi ya chikondwerero cha mwezi wa Etanimu, mwezi wachisanu ndi chiwiri. Onani mutuwo |