Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 2:7 - Buku Lopatulika

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Yesu adauza anyamata aja kuti, “Dzazani mbiyazi ndi madzi.” Ndipo adazidzaza mpaka m'milomo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu anati kwa antchitowo, “Dzazani madzi mʼmitsukoyi,” ndipo iwo anadzaza ndendende.

Onani mutuwo



Yohane 2:7
12 Mawu Ofanana  

Ndipo Eliya anati kwa iye, Usachita mantha, kachite monga umo wanenamo, koma yamba wandiotcherako kamkate, nubwere nako kwa ine; ndipo utatero udziphikire wekha ndi mwana wako.


Ndipo pakutha vinyo, amake wa Yesu ananena naye, Alibe vinyo.


Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.


Ndipo panali pamenepo mitsuko yamiyala isanu ndi umodzi yoikidwako monga mwa mayeretsedwe a Ayuda, yonse ya miyeso iwiri kapena itatu.


Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.