Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 2:5 - Buku Lopatulika

5 Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Apo amai ake adauza anyamata amene ankatumikira kuti, “Chilichonse chimene akuuzeni, muchite.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Amayi ake anati kwa antchito, “Inu muchite chilichonse chimene akuwuzeni.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 2:5
12 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene dziko lonse la Ejipito linali ndi njala, anthu anafuulira Farao awapatse chakudya; ndipo Farao anati kwa Aejipito onse, Pitani kwa Yosefe: chimene iye anena kwa inu chitani.


Chotero anachita Nowa, monga mwa zonse anamlamulira iye Mulungu, momwemo anachita.


Ndipo ndinachita monga momwe anandilamulira, ndinatulutsa akatundu anga usana, ngati a pa ulendo wa kundende, ndi madzulo ndinaboola pakhoma ndi dzanja langa, ndinawatulutsa pali mdima, ndi kuwasenza paphewa panga pamaso pao.


Pamene Iye anali chilankhulire ndi makamu, onani, amake ndi abale ake anaima panja, nafuna kulankhula naye.


Muli abwenzi anga inu, ngati muzichita zimene ndikulamulani inu.


komatu, uka, nulowe m'mzinda, ndipo kudzanenedwa kwa iwe chimene uyenera kuchita.


Ndi chikhulupiriro Abrahamu, poitanidwa, anamvera kutuluka kunka kumalo amene adzalandira ngati cholowa; ndipo anatuluka wosadziwa kumene akamukako.


ndipo pamene anakonzeka wamphumphu anakhala kwa onse akumvera Iye chifukwa cha chipulumutso chosatha;


Chilichonse chichokera kumpesa asadyeko, asamwe vinyo kapena choledzeretsa, kapena kudya chilichonse chodetsa; zonse ndinamlamulira azisunge.


Pamenepo anatsikira popunthirapo, nachita zonse monga umo mpongozi wake adamuuza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa