Yohane 2:5 - Buku Lopatulika5 Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Apo amai ake adauza anyamata amene ankatumikira kuti, “Chilichonse chimene akuuzeni, muchite.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Amayi ake anati kwa antchito, “Inu muchite chilichonse chimene akuwuzeni.” Onani mutuwo |