Yohane 2:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Pambuyo pake adaŵauza kuti, “Tsopano tungani, kaperekeni kwa mkulu wa phwando,” Iwowo adakaperekadi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndipo Iye anatinso kwa iwo, “Tsopano tungani ndipo kaperekeni kwa mkulu waphwando.” Iwo anachita momwemo. Onani mutuwo |