Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 2:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Pambuyo pake adaŵauza kuti, “Tsopano tungani, kaperekeni kwa mkulu wa phwando,” Iwowo adakaperekadi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ndipo Iye anatinso kwa iwo, “Tsopano tungani ndipo kaperekeni kwa mkulu waphwando.” Iwo anachita momwemo.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 2:8
5 Mawu Ofanana  

Chikondi chao ndi mdano wao ndi dumbo lao lomwe zatha tsopano; ndipo nthawi yamuyaya sagawa konse kanthu kalikonse kachitidwe pansi pano.


Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende.


Koma pamene mkuluyo analawa madzi osanduka vinyowo, ndipo sanadziwe kumene anachokera (koma atumiki amene adatunga madzi anadziwa), mkuluyo anaitana mkwati,


Perekani kwa anthu onse mangawa ao; msonkho kwa eni ake a msonkho; kulipira kwa eni ake a kulipidwa; kuopa kwa eni ake a kuwaopa; ulemu kwa eni ake a ulemu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa