Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 11:7 - Buku Lopatulika

Ndipo pambuyo pake ananena kwa ophunzira ake, Tiyeni tipitenso ku Yudeya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pambuyo pake ananena kwa ophunzira ake, Tiyeni tipitenso ku Yudeya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake adauza ophunzira ake kuti, “Tiyeni tipitenso ku Yudeya.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka anati kwa ophunzira ake, “Tiyeni tibwerere ku Yudeya.”

Onani mutuwo



Yohane 11:7
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pa kubadwa kwake kwa Yesu mu Betelehemu wa Yudeya m'masiku a Herode mfumu, onani, Anzeru a kum'mawa anafika ku Yerusalemu,


Ndipo panali, pamene anayamba kukwanira masiku akuti alandiridwe Iye kumwamba, Yesu anatsimikiza kuloza nkhope yake kunka ku Yerusalemu,


Chifukwa chake pamene anamva kuti anadwala, anakhala pamenepo pamalo pomwepo masiku awiri.


Patapita masiku, Paulo anati kwa Barnabasi, Tibwerere, tizonde abale m'mizinda yonse m'mene tinalalikiramo mau a Ambuye, tione mkhalidwe wao.