Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Yohane 1:2 - Buku Lopatulika

Awa anali pachiyambi kwa Mulungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Awa anali pachiyambi kwa Mulungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anali kwa Mulungu chikhalire.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mawuwa anali ndi Mulungu pachiyambi.

Onani mutuwo



Yohane 1:2
5 Mawu Ofanana  

Pachiyambi Mulungu adalenga kumwamba ndi dziko lapansi.


Ndinali pa mbali pake ngati mmisiri; ndinamsekeretsa tsiku ndi tsiku, ndi kukondwera pamaso pake nthawi zonse;


Ndipo ngati nditi, Sindidzamtchula Iye, sindidzanenanso m'dzina lake, pamenepo m'mtima mwanga muli ngati moto wotentha wotsekedwa m'mafupa anga, ndipo ndalema ndi kupirira, sindingathe kupiriranso.


Pachiyambi panali Mau, ndipo Mau anali kwa Mulungu, ndipo Mau ndiye Mulungu.


Zonse zinalengedwa ndi Iye; ndipo kopanda Iye sikunalengedwe kanthu kalikonse kolengedwa.