Yeremiya 20:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo ngati nditi, Sindidzamtchula Iye, sindidzanenanso m'dzina lake, pamenepo m'mtima mwanga muli ngati moto wotentha wotsekedwa m'mafupa anga, ndipo ndalema ndi kupirira, sindingathe kupiriranso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo ngati nditi, Sindidzamtchula Iye, sindidzanenanso m'dzina lake, pamenepo m'mtima mwanga muli ngati moto wotentha wotsekedwa m'mafupa anga, ndipo ndalema ndi kupirira, sindingathe kupiriranso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndikanena kuti, “Sindidzalalikanso za Chauta, sindidzalankhulanso m'dzina lake,” mau anu, Inu Chauta, amayaka ngati moto mumtima mwanga. Ndimayesa kuŵasunga m'kati, koma pambuyo pake ndimaŵatulutsa popeza kuti sindingathe kupirira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma ndikanena kuti, “Sindidzalalikiranso za Iye kapena kuyankhulanso mʼdzina lake,” mawu anu amayaka ngati moto mu mtima mwanga, amakhaladi ngati moto wotsekeredwa mʼmafupa anga. Ndapirira kusunga mawu anu mu mtima mwanga osawatulutsa, koma sindingathe kupirirabe. Onani mutuwo |