Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:66 - Buku Lopatulika

Tsiku lakhumi kalonga wa ana a Dani, ndiye Ahiyezere mwana wa Amisadai:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsiku lakhumi kalonga wa ana a Dani, ndiye Ahiyezere mwana wa Amisadai:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsiku lakhumi linali la Ahiyezere mwana wa Amishadai, mtsogoleri wa Adani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa tsiku lakhumi Ahiyezeri mwana wa Amisadai, mtsogoleri wa fuko la Dani anabweretsa chopereka chake.

Onani mutuwo



Numeri 7:66
2 Mawu Ofanana  

Wa Dani, Ahiyezere mwana wa Amisadai.


Mbendera ya chigono cha Dani izikhala kumpoto monga mwa makamu ao; ndi kalonga wa ana a Dani ndiye Ahiyezere mwana wa Amisadai.