Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:5 - Buku Lopatulika

Uzilandira kwa iwo, kuti zikhale zakuchitira ntchito ya chihema chokomanako; nuzipereke kwa Alevi, yense monga mwa ntchito yake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Uzilandira kwa iwo, kuti zikhale zakuchitira ntchito ya chihema chokomanako; nuzipereke kwa Alevi, yense monga mwa ntchito yake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Ulandire zimenezi kwa anthuwo kuti zithandize potumikira m'chihema chamsonkhano. Uŵapatse Alevi zimenezo, aliyense zoyenera ntchito yake.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Ulandire zimenezi kwa iwo kuti zigwire ntchito ku tenti ya msonkhano. Uzipereke kwa Alevi, aliyense monga mwa ntchito yake.”

Onani mutuwo



Numeri 7:5
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,


Ndipo Mose analandira magaleta ndi ng'ombe, nazipereka kwa Alevi.


Okhulupirika mauwa, ndipo za izi ndifuna kuti ulimbitse mau, kuti iwo akukhulupirira Mulungu asamalire akhalebe atsogoleri a ntchito zabwino. Izi nzokoma ndi zopindulitsa anthu;