Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 7:5 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 “Ulandire zimenezi kwa iwo kuti zigwire ntchito ku tenti ya msonkhano. Uzipereke kwa Alevi, aliyense monga mwa ntchito yake.”

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

5 Uzilandira kwa iwo, kuti zikhale zakuchitira ntchito ya chihema chokomanako; nuzipereke kwa Alevi, yense monga mwa ntchito yake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Uzilandira kwa iwo, kuti zikhale zakuchitira ntchito ya chihema chokomanako; nuzipereke kwa Alevi, yense monga mwa ntchito yake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 “Ulandire zimenezi kwa anthuwo kuti zithandize potumikira m'chihema chamsonkhano. Uŵapatse Alevi zimenezo, aliyense zoyenera ntchito yake.”

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:5
9 Mawu Ofanana  

Yehova anawuza Mose kuti,


Choncho Mose anatenga ngolo ndi ngʼombe zothenazo nazipereka kwa Alevi.


Mawuwa ndi okhulupirika ndipo ine ndikufuna kuti iwe utsindike zinthu izi, kuti amene akhulupirira Mulungu adzipereke kuchita ntchito zabwino. Zinthu izi ndi zabwino kwambiri ndi zopindulitsa kwa aliyense.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa