Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:42 - Buku Lopatulika

Tsiku lachisanu ndi chimodzi kalonga wa ana a Gadi, Eliyasafu mwana wa Deuwele:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsiku lachisanu ndi chimodzi kalonga wa ana a Gadi, Eliyasafu mwana wa Deuwele:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsiku lachisanu ndi chimodzi linali la Eliyasafu mwana wa Deuwele mtsogoleri wa Agadi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa tsiku lachisanu ndi chimodzi, Eliyasafu mwana wa Deuweli, mtsogoleri wa fuko la Gadi, anabweretsa chopereka chake.

Onani mutuwo



Numeri 7:42
4 Mawu Ofanana  

Wa Gadi, Eliyasafu mwana wa Deuwele.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Gadi anayang'anira Eliyasafu mwana wa Deuwele.


Ndi fuko la Gadi; kalonga wa ana a Gadi ndiye Eliyasafu mwana wa Reuwele.


ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Selumiele mwana wa Zurishadai.