Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 7:30 - Buku Lopatulika

Tsiku lachinai Elizuri, mwana wa Sedeuri, kalonga wa ana a Rubeni:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tsiku lachinai Elizuri, mwana wa Sedeuri, kalonga wa ana a Rubeni:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsiku lachinai linali la Elizuri mwana wa Sedeuri, mtsogoleri wa Arubeni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsiku lachinayi linali la Elizuri mwana wa Sedeuri, mtsogoleri wa fuko la Rubeni, anabweretsa chopereka chake.

Onani mutuwo



Numeri 7:30
4 Mawu Ofanana  

Ndipo maina a amuna amene aime nanu ndi awa: wa Rubeni, Elizuri mwana wa Sedeuri.


Mbendera ya chigono cha Rubeni ikhale kumwera monga mwa makamu ao; ndipo kalonga wa ana a Rubeni ndiye Elizuri mwana wa Sedeuri.


ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Eliyabu mwana wa Heloni.


chopereka chake ndicho mbale imodzi yasiliva, kulemera kwake masekeli zana limodzi ndi makumi atatu, mbale yowazira imodzi yasiliva ya masekeli makumi asanu ndi awiri, kuyesa sekeli wa malo opatulika, zonse ziwiri zodzaza ndi ufa wosakaniza ndi mafuta, ukhale nsembe yaufa;