Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 7:29 - Buku Lopatulika

29 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Ndipo zoperekera nsembe yachiyanjano zinali ng'ombe ziŵiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, ndi anaankhosa asanu amphongo a chaka chimodzi. Zimenezi ndizo zinali zopereka za Eliyabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 ndi ngʼombe ziwiri, nkhosa zazimuna zisanu, mbuzi zazimuna zisanu ndi ana ankhosa aamuna asanu a chaka chimodzi, nsembe yachiyanjano. Ichi chinali chopereka cha Eliabu mwana wa Heloni.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 7:29
4 Mawu Ofanana  

Wa Zebuloni, Eliyabu mwana wa Heloni.


Ndi fuko la Zebuloni: kalonga wa ana a Zebuloni ndiye Eliyabu mwana wa Heloni.


tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo;


Tsiku lachinai Elizuri, mwana wa Sedeuri, kalonga wa ana a Rubeni:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa