Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 4:42 - Buku Lopatulika

Ndipo owerengedwa a mabanja a ana a Merari, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo owerengedwa a mabanja a ana a Merari, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaŵerenganso ana a Merari potsata mabanja ao ndiponso banja la makolo ao,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amerari anawawerenga monga mwa mafuko ndi mabanja awo.

Onani mutuwo



Numeri 4:42
4 Mawu Ofanana  

mwana wa Mali, mwana wa Musi, mwana wa Merari, mwana wa Levi.


ndi iwo oyesedwa mwa chibadwidwe cha ansembe mwa nyumba za makolo ao, ndi Alevi, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu mu udikiro mwao, monga mwa zigawo zao;


Amenewo ndiwo owerengedwa a mabanja a ana a Geresoni, onse akutumikira m'chihema chokomanako, adawawerenga Mose ndi Aroni monga mwa mau a Yehova.


kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu kufikira a zaka makumi asanu, onse akulowa utumikiwu kuti agwire ntchito m'chihema chokomanako,