Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 4:40 - Buku Lopatulika

owerengedwa ao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

owerengedwa ao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chiŵerengero chao chidakwanira 2,630 potsata mabanja ao ndiponso banja la makolo ao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

atawawerenga mwa mafuko ndi mabanja awo, anali 2,630.

Onani mutuwo



Numeri 4:40
3 Mawu Ofanana  

Ndipo kalonga wa akalonga a Alevi ndiye Eleazara mwana wa Aroni wansembeyo; ndiye aziyang'anira osunga udikiro wa pamalo opatulika.


kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu kufikira a zaka makumi asanu, onse akulowa utumikiwu, kuti agwire ntchito m'chihema chokomanako,


Amenewo ndiwo owerengedwa a mabanja a ana a Geresoni, onse akutumikira m'chihema chokomanako, adawawerenga Mose ndi Aroni monga mwa mau a Yehova.