Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 4:38 - Buku Lopatulika

Ndipo ana owerengedwa a Geresoni, monga mwa mabanja ao, ndi monga mwa nyumba za makolo ao,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ana owerengedwa a Geresoni, monga mwa mabanja ao, ndi monga mwa nyumba za makolo ao,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Adaŵerenganso ana a Geresoni potsata mabanja ao ndiponso banja la makolo ao,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ageresoni anawerengedwanso monga mwa mafuko ndi mabanja awo.

Onani mutuwo



Numeri 4:38
4 Mawu Ofanana  

ndi iwo oyesedwa mwa chibadwidwe cha ansembe mwa nyumba za makolo ao, ndi Alevi, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu mu udikiro mwao, monga mwa zigawo zao;


Owerengedwa ao, powawerenga amuna onse, kuyambira mwana wa mwezi umodzi ndi mphambu, owerengedwa ao ndiwo zikwi zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.


Awa ndi owerengedwa a mabanja a Akohati, onse akutumikira m'chihema chokomanako, amene Mose ndi Aroni anawawerenga monga mwa mau a Yehova mwa dzanja la Mose.


kuyambira a zaka makumi atatu ndi mphambu kufikira a zaka makumi asanu, onse akulowa utumikiwu, kuti agwire ntchito m'chihema chokomanako,