Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 33:5 - Buku Lopatulika

Ndipo ana a Israele anachokera ku Ramsesi, nayenda namanga ku Sukoti.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ana a Israele anachokera ku Ramsesi, nayenda namanga ku Sukoti.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pambuyo pake Aisraele adanyamuka ku Ramsesi nakamanga mahema ku Sukoti.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aisraeli atachoka ku Ramesesi, anamanga misasa yawo ku Sukoti.

Onani mutuwo



Numeri 33:5
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ana a Israele anayenda ulendo wakuchokera ku Ramsesi kufikira ku Sukoti, zikwi mazana asanu ndi limodzi oyenda okha, ndiwo amuna, osawerenga ana.


Nachokera ku Sukoti, nayenda namanga mu Etamu, ndiko ku malekezero a chipululu.