Eksodo 12:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo ana a Israele anayenda ulendo wakuchokera ku Ramsesi kufikira ku Sukoti, zikwi mazana asanu ndi limodzi oyenda okha, ndiwo amuna, osawerenga ana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo ana a Israele anayenda ulendo wakuchokera ku Ramsesi kufikira ku Sukoti, zikwi mazana asanu ndi limodzi oyenda okha, ndiwo amuna, osawerenga ana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Tsono Aisraele adanyamuka ulendo kuchoka ku Ramsesi kupita ku Sukoti. Anthu aamuna analipo zikwi 600, osaŵerenga akazi ndi ana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Aisraeli anayenda ulendo kuchokera ku Ramesesi mpaka kukafika ku Sukoti. Anthu aamuna oyenda pansi analipo 600,000 osawerengera akazi ndi ana. Onani mutuwo |