Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 32:31 - Buku Lopatulika

Ndipo ana a Gadi ndi ana a Rubeni anayankha, nati, Monga Yehova anati kwa anyamata anu momwemo tidzachita.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ana a Gadi ndi ana a Rubeni anayankha, nati, Monga Yehova anati kwa anyamata anu momwemo tidzachita.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo zidzukulu za Gadi ndi za Rubeni zidayankha kuti, “Ife atumiki anu tidzachita zomwe Chauta watiwuza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Agadi ndi Arubeni anayankha kuti, “Antchito anu adzachita zimene Yehova wanena.

Onani mutuwo



Numeri 32:31
4 Mawu Ofanana  

koma akapanda kuoloka nanu okonzeka, akhale nao maiko aoao pakati pa inu m'dziko la Kanani.


Tidzaoloka okonzeka pamaso pa Yehova ku dziko la Kanani, koma cholowa chathuchathu chikhale tsidya lino la Yordani.


Rubeni akhale ndi moyo, asafe, koma amuna ake akhale owerengeka.


Ndipo anamyankha Yoswa, nati, Zonse mwatilamulira tidzachita, ndipo kulikonse mutitumako tidzamuka.