Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 3:48 - Buku Lopatulika

nupereke ndalama zimene akuposawo anaomboledwa nazo kwa Aroni ndi kwa ana ake aamuna.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nupereke ndalama zimene akuposawo anaomboledwa nazo kwa Aroni ndi kwa ana ake amuna.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Upatse Aroni pamodzi ndi ana ake aamuna ndalama zimenezi, kuti zikhale mtengo woombolera Aisraele a chiŵerengero chopitirira chija.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndalama zimenezi uzipereke kwa Aaroni ndi ana ake aamuna kuti ukhale mtengo woombolera Aisraeli woonjezerawo.”

Onani mutuwo



Numeri 3:48
3 Mawu Ofanana  

ulandire masekeli asanu pa munthu mmodzi; uwalandire pa muyeso wa sekeli wa malo opatulika (sekeli ndiwo magera makumi awiri);


Pamenepo Mose analandira ndalama zoombola nazo kwa iwo akuposa aja adawaombola Alevi;


Ndipo Mose anapatsa Aroni ndi ana ake ndalama zoombola nazo monga mwa mau a Yehova, monga Yehova adauza Mose.