Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 3:26 - Buku Lopatulika

ndi nsalu zotchinga za kubwalo, ndi nsalu yotsekera pa chipata cha pabwalo, lokhala ku chihema, ndi ku guwa la nsembe pozungulira, ndi zingwe zake za ku ntchito zake zonse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi nsalu zotchinga za kubwalo, ndi nsalu yotsekera pa chipata cha pabwalo, lokhala ku Kachisi, ndi ku guwa la nsembe pozungulira, ndi zingwe zake za ku ntchito zake zonse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

nsalu zochingira bwalo, nsalu zochingira khomo la bwalo lozungulira chihema cha Mulungu ndi guwa lansembe, ndiponso zingwe zake. Ankagwira ntchito zonse zokhudza zimenezi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndi makatani wotchinga bwalo, katani ya pa chipata cholowera ku bwalo lozungulira Chihema ndi guwa lansembe, zingwe ndi zonse zokhudzana ndi ntchito yawo.

Onani mutuwo



Numeri 3:26
5 Mawu Ofanana  

zichiri za chihema, ndi zichiri za kubwalo, ndi zingwe zao;


Banja la Aamuramu, ndi banja la Aizihara, ndi banja la Ahebroni, ndi banja la Auziyele ndiwo a Kohati; ndiwo mabanja a Akohati.


Ntchito ya mabanja a Ageresoni, pogwira ntchito ndi kusenza katundu ndi iyi;