Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 3:22 - Buku Lopatulika

Owerengedwa ao, powawerenga amuna onse, kuyambira mwana wa mwezi umodzi ndi mphambu, owerengedwa ao ndiwo zikwi zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Owerengedwa ao, powawerenga amuna onse, kuyambira mwana wa mwezi umodzi ndi mphambu, owerengedwa ao ndiwo zikwi zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chiŵerengero chao potsata kuchuluka kwa amuna onse, kuyambira mwana wamwamuna wa mwezi umodzi ndi wopitirapo, chinali 7,500.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chiwerengero cha amuna onse amene anawawerenga a mwezi umodzi kapena kupitirirapo chinali 7,500.

Onani mutuwo



Numeri 3:22
3 Mawu Ofanana  

Banja la Libini, ndi mabanja a Simei, ndiwo a Geresoni; ndiwo mabanja a Geresoni.


Mabanja a Ageresoni azimanga mahema ao pambuyo pa chihema kumadzulo.