Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 3:22 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Chiwerengero cha amuna onse amene anawawerenga a mwezi umodzi kapena kupitirirapo chinali 7,500.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

22 Owerengedwa ao, powawerenga amuna onse, kuyambira mwana wa mwezi umodzi ndi mphambu, owerengedwa ao ndiwo zikwi zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Owerengedwa ao, powawerenga amuna onse, kuyambira mwana wa mwezi umodzi ndi mphambu, owerengedwa ao ndiwo zikwi zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Chiŵerengero chao potsata kuchuluka kwa amuna onse, kuyambira mwana wamwamuna wa mwezi umodzi ndi wopitirapo, chinali 7,500.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 3:22
3 Mawu Ofanana  

Kwa Geresoni kunali banja la Alibini, banja la Asimei. Amenewa ndiwo anali mabanja a Ageresoni.


Mabanja a Ageresoni azimanga misasa yawo kumadzulo, kumbuyo kwa Chihema.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa