Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 3:17 - Buku Lopatulika

Ndipo ana a Levi maina ao ndi awa: Geresoni, ndi Kohati ndi Merari.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ana a Levi maina ao ndi awa: Geresoni, ndi Kohati ndi Merari.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Maina a ana a Leviwo ndi aŵa: Geresoni, Kohati ndi Merari.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mayina a ana aamuna a Levi ndi awa: Geresoni, Kohati ndi Merari.

Onani mutuwo



Numeri 3:17
12 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Levi: Geresoni, Kohati, ndi Merari.


Ndipo Davide anawagawa magawo monga mwa ana a Levi: Geresoni, Kohati, ndi Merari.


Ndipo Mose anawawerenga monga mwa mau a Yehova, monga adamuuza.