Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 27:9 - Buku Lopatulika

Ndipo akapanda kukhala naye mwana wamkazi, mupatse abale ake cholowa chake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo akapanda kukhala naye mwana wamkazi, mupatse abale ake cholowa chake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akakhala kuti alibe mwana wamkazi, choloŵa chakecho chikhale cha abale ake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati alibe mwana wamkazi, muzipereka cholowa chakecho kwa abale ake.

Onani mutuwo



Numeri 27:9
2 Mawu Ofanana  

Ndipo akapanda kukhala nao abale, mupatse abale a atate wake cholowa chake.


Ndipo unene ndi ana a Israele, ndi kuti, Akafa munthu wamwamuna wopanda mwana wamwamuna, cholowa chake achilandire mwana wake wamkazi.