Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 27:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ngati alibe mwana wamkazi, muzipereka cholowa chakecho kwa abale ake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

9 Ndipo akapanda kukhala naye mwana wamkazi, mupatse abale ake cholowa chake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo akapanda kukhala naye mwana wamkazi, mupatse abale ake cholowa chake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Akakhala kuti alibe mwana wamkazi, choloŵa chakecho chikhale cha abale ake.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 27:9
2 Mawu Ofanana  

Ngati alibe abale muzipereka cholowa chake kwa abale a abambo ake.


“Uza Aisraeli kuti, ‘Ngati munthu afa wosasiya mwana wamwamuna, muzipereka cholowa chake kwa mwana wake wamkazi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa