Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:8 - Buku Lopatulika

Mwana wamwamuna wa Palu ndiye Eliyabu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mwana wamwamuna wa Palu ndiye Eliyabu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mwana wa Palu anali Eliyabu,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mwana wa Palu anali Eliabu,

Onani mutuwo



Numeri 26:8
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Rubeni: Hanoki, ndi Palu, ndi Hezironi, ndi Karimi.


Iwo ndiwo mabanja a Arubeni; owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi anai mphambu zitatu kudza mazana asanu ndi awiri mphambu makumi atatu.


Ndi ana a Eliyabu: Nemuwele, ndi Datani ndi Abiramu. Iwo ndiwo Datani ndi Abiramu omwe aja oitanidwa a khamu, amene anatsutsana ndi Mose ndi Aroni mu msonkhano wa Kora, muja anatsutsana ndi Yehova;