Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:46 - Buku Lopatulika

Ndipo dzina la mwana wamkazi wa Asere ndiye Sera.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo dzina la mwana wamkazi wa Asere ndiye Sera.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mwana wamkazi wa Asere anali Sera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

(Aseri anali ndi mwana wamkazi dzina lake Sera)

Onani mutuwo



Numeri 26:46
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Asere: Imina, ndi Isiva, ndi Isivi, ndi Beriya, ndi Sera mlongo wao; ndi ana a Beriya: Hebere, ndi Malikiele.


Ana a Beriya ndiwo: Hebere, ndiye kholo la banja la Ahebere; Malikiele, ndiye kholo la banja la Amalikiele.


Iwo ndiwo mabanja a ana aamuna a Asere monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.