Genesis 46:17 - Buku Lopatulika17 Ndi ana aamuna a Asere: Imina, ndi Isiva, ndi Isivi, ndi Beriya, ndi Sera mlongo wao; ndi ana a Beriya: Hebere, ndi Malikiele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndi ana amuna a Asere: Imina, ndi Isiva, ndi Isivi, ndi Beriya, ndi Sera mlongo wao; ndi ana a Beriya: Hebere, ndi Malikiele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ana a Asere anali aŵa: Imina, Isiva, Isivi, Beriya ndi mlongo wao Sera. Ana a Beriya anali aŵa: Hebere ndi Malikiele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Ana aamuna a Aseri ndi awa: Imuna, Isiva, Isivi, Beriya ndi Sera mlongo wawo. Ana aamuna a Beriya ndi awa: Heberi ndi Malikieli. Onani mutuwo |