Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:32 - Buku Lopatulika

ndi Semida, ndiye kholo la banja la Asemida; ndi Hefere, ndiye kholo la banja la Ahefere.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Semida, ndiye kholo la banja la Asemida; ndi Hefere, ndiye kholo la banja la Ahefere.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Semida anali kholo la banja la Asemida. Hefere anali kholo la banja la Ahefere.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kuchokera mwa Semida, fuko la Asemida; kuchokera mwa Heferi, fuko la Aheferi.

Onani mutuwo



Numeri 26:32
3 Mawu Ofanana  

ndi Asiriele, ndiye kholo la banja la Aasiriele; ndi Sekemu, ndiye kholo la banja la Asekemu;


Ndipo Zelofehadi mwana wa Hefere analibe ana aamuna, koma ana aakazi ndiwo; ndipo maina a ana aakazi a Zelofehadi ndiwo Mala ndi Nowa, Hogila, Milika ndi Tiriza.


Ndipo maere anagwera ana ena otsala a Manase monga mwa mabanja ao; ana a Abiyezere ndi ana a Heleki, ndi ana a Asiriele, ndi ana a Sekemu ndi ana a Hefere, ndi ana a Semida; awa ndi ana aamuna a Manase mwana wa Yosefe, monga mwa mabanja ao.