Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:24 - Buku Lopatulika

Yasubu, ndiye kholo la banja la Ayasubu; Simironi, ndiye kholo la banja la Asimironi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Yasubu, ndiye kholo la banja la Ayasubu; Simironi, ndiye kholo la banja la Asimironi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yasubu anali kholo la banja la Ayasubu. Simeoni anali kholo la banja la Asimeoni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kuchokera mwa Yasubu, fuko la Ayasubu. Kuchokera mwa Simironi, fuko la Asimironi.

Onani mutuwo



Numeri 26:24
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Isakara: Tola ndi Puva, ndi Iyobu, ndi Simironi.


Ana aamuna a Isakara monga mwa mabanja ao ndiwo: Tola, ndiye kholo la banja la Atola; Puva, ndiye kholo la banja la Apuni;


Iwo ndiwo mabanja a Isakara monga mwa owerengedwa ao; zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana atatu.