Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 26:17 - Buku Lopatulika

Arodi, ndiye kholo la banja la Aarodi; Areli, ndiye kholo la banja la Aareli.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Arodi, ndiye kholo la banja la Aarodi; Areli, ndiye kholo la banja la Aareli.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Arodi anali kholo la banja la Aarodi. Areli anali kholo la banja la Aareli.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

kuchokera mwa Arodi, fuko la Aarodi; kuchokera mwa Arieli, fuko la a Areli.

Onani mutuwo



Numeri 26:17
3 Mawu Ofanana  

Ndi ana aamuna a Gadi: Zifiyoni, ndi Hagi, ndi Suni, ndi Eziboni, ndi Eri, ndi Arodi, ndi Areli.


Ozini, ndiye kholo la banja la Aozini; Eri, ndiye kholo la banja la Aeri;


Iwo ndiwo mabanja a ana a Gadi, monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi anai ndi mazana asanu.