Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 21:15 - Buku Lopatulika

ndi zigwa za miyendoyo zakutsikira kwao kwa Ari, ndi kuyandikizana ndi malire a Mowabu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi zigwa za miyendoyo zakutsikira kwao kwa Ari, ndi kuyandikizana ndi malire a Mowabu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ku matsitso a zigwa amene afika mpaka ku Ari, nakhudza malire a dziko la Mowabu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ku matsitso a zigwa amene afika mpaka ku Ari nakhudza malire a dziko la Mowabu.”

Onani mutuwo



Numeri 21:15
6 Mawu Ofanana  

Katundu wa Mowabu. Pakuti usiku umodzi Ari wa ku Mowabu wapasuka, nakhala chabe; usiku umodzi Kiri wa Mowabu wapasuka, nakhala chabe.


Chifukwa chake, ananena m'buku la Nkhondo za Yehova, Waheba mu Sufa, ndi miyendo ya Arinoni;


Popeza moto unatuluka mu Hesiboni, chirangali cha moto m'mzinda wa Sihoni; chatha Ari wa Mowabu, eni misanje ya Arinoni.


Lero lomwe utumphe malire a Mowabu, ndiwo Ari.


monga anandichitira ana a Esau akukhala mu Seiri, ndi Amowabu akukhala mu Ari; kufikira nditaoloka Yordani kulowa dziko limene Yehova Mulungu wathu atipatsa.


Ndipo Yehova anati kwa ine, Usavuta Mowabu, kapena kuutsana naye nkhondo; popeza sindidzakupatsako dziko lake likhale lakolako; pakuti ndinapatsa ana a Loti Ari likhale laolao.