Numeri 21:14 - Buku Lopatulika14 Chifukwa chake, ananena m'buku la Nkhondo za Yehova, Waheba mu Sufa, ndi miyendo ya Arinoni; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Chifukwa chake, ananena m'buku la Nkhondo za Yehova, Waheba m'Sufa, ndi miyendo ya Arinoni; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Nchifukwa chake buku la nkhondo za Chauta limanena kuti, “Mzinda wa Waheba uli ku Sufa, ku zigwa za Arinoni, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Nʼchifukwa chake Buku la Nkhondo za Yehova limati, “Mzinda wa Wahebu uli mu Sufa, mu zigwa za Arinoni, Onani mutuwo |