Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 2:30 - Buku Lopatulika

Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndipo ankhondo ake ngokwanira 53,400.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 53,400.

Onani mutuwo



Numeri 2:30
4 Mawu Ofanana  

Ndi fuko la Nafutali: ndi kalonga wa ana a Nafutali ndiye Ahira mwana wa Enani.


Owerengedwa onse a chigono cha Dani ndiwo zikwi makumi khumi mphambu makumi asanu kudza zisanu ndi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi. Iwo ndiwo aziyenda m'mbuyo paulendo, monga mwa mbendera zao.


Iwo ndiwo mabanja a Nafutali, monga mwa mabanja ao; ndipo owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana anai.