Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 2:30 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 53,400.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

30 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 ndipo ankhondo ake ngokwanira 53,400.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:30
4 Mawu Ofanana  

Lotsatira lidzakhala fuko la Nafutali. Mtsogoleri wa Anafutali ndi Ahira mwana wa Enani.


Anthu onse aamuna mu msasa wa Dani chiwerengero chawo ndi 157,600. Iwo azidzanyamuka pomaliza, ndi mbendera zawo.


Awa ndiwo anali mafuko a Nafutali. Onse amene anawerengedwa analipo 45,400.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa