Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 15:18 - Buku Lopatulika

Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Pamene mulowa m'dziko limene ndilikukulowetsani,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Pamene mulowa m'dziko limene ndilikukulowetsani,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Uza Aisraele kuti, ‘Mukadzaloŵa m'dziko m'mene ndidzakufikitsani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Yankhula ndi Aisraeli ndipo unene kuti, ‘Mukakalowa mʼdziko limene ndikukutengeraniko

Onani mutuwo



Numeri 15:18
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


kudzali, pakudya inu mkate wa m'dzikolo, muzikwezera Yehova nsembe yokweza.


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mukakalowa m'dziko lokakhalamo inu, limene ndilikupatsa inu,


Ndipo ngati zipatso zoyamba zili zopatulika, choteronso mtanda; ndipo ngati muzu uli wopatulika, choteronso nthambi.