Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 15:19 - Buku Lopatulika

19 kudzali, pakudya inu mkate wa m'dzikolo, muzikwezera Yehova nsembe yokweza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 kudzali, pakudya inu mkate wa m'dzikolo, muzikwezera Yehova nsembe yokweza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 ndipo mukamadzadya buledi wam'dzikolo, mudzapereke nsembe kwa Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 ndipo mukakadya chakudya cha mʼdzikolo, mukapereke gawo lina kwa Yehova monga chopereka.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 15:19
3 Mawu Ofanana  

Ndipo wansembe mwana wa Aroni azikhala ndi Alevi, polandira Alevi limodzilimodzi la magawo khumi; ndi Alevi azikwera nalo limodzi la magawo khumi mwa limodzilimodzi la magawo khumi kunyumba ya Mulungu wathu, kuzipinda, kunyumba ya chuma.


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Pamene mulowa m'dziko limene ndilikukulowetsani,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa