Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 14:26 - Buku Lopatulika

Ndipo Yehova ananena kwa Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yehova ananena kwa Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chauta adafunsa Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yehova anawuza Mose ndi Aaroni kuti,

Onani mutuwo



Numeri 14:26
3 Mawu Ofanana  

Koma Aamaleke ndi Akanani akhala m'chigwamo; tembenukani mawa, nimunke ulendo wanu kuchipululu, njira ya ku Nyanja Yofiira.


Ndileke khamu loipa ili lakudandaula pa Ine kufikira liti? Ndidamva madandaulo a ana a Israele, amene amandidandaulira.


Popeza Yehova adanena za iwowa, Adzafatu m'chipululu. Ndipo sanatsalire mmodzi wa iwowa koma Kalebe mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni.