Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 13:25 - Buku Lopatulika

Pamenepo anabwerera atazonda dziko, atatha masiku makumi anai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo anabwerera atazonda dziko, atatha masiku makumi anai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Patapita masiku makumi anai, anthu aja adabwerako kumene adakazonda dziko kuja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Patapita masiku makumi anayi, anthu aja anabwerako kokazonda dziko lija.

Onani mutuwo



Numeri 13:25
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose analowa m'kati mwa mtambo, nakwera m'phirimo; ndipo Mose anakhala m'phiri masiku makumi anai usana ndi usiku.


Ndipo anakhala pomwepo ndi Yehova masiku makumi anai, usana ndi usiku; sanadye mkate kapena kumwa madzi. Ndipo analembera pa magomewo mau a panganolo, mau khumiwo.


Malowa anawatcha chigwa cha Esikolo, chifukwa cha tsangolo ana a Israele analichekako.


Ndipo anamuka, nadza kwa Mose, ndi Aroni, ndi khamu lonse la ana a Israele, ku chipululu cha Parani ku Kadesi; ndipo anabwezera mau iwowa, ndi khamu lonse, nawaonetsa zipatso za dzikoli.