Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 13:24 - Buku Lopatulika

Malowa anawatcha chigwa cha Esikolo, chifukwa cha tsangolo ana a Israele analichekako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Malowa anawatcha chigwa cha Esikolo, chifukwa cha tsangolo ana a Israele analichekako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Malowo adaŵatcha chigwa cha Esikolo, chifukwa cha tsango lamphesa limene anthu aja adathyola kumeneko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Malo amenewo anawatcha chigwa cha Esikolo chifukwa cha phava la mphesa limene Aisraeli anadula kumeneko.

Onani mutuwo



Numeri 13:24
3 Mawu Ofanana  

Ndipo anadza ku chigwa cha Esikolo, nachekako tsango limodzi la mphesa, nalisenza awiri mopika; anabwera nazonso makangaza ndi nkhuyu.


Pamenepo anabwerera atazonda dziko, atatha masiku makumi anai.


Popeza atakwera kunka ku chigwa cha Esikolo, naona dziko, anafoketsa mtima wa ana a Israele, kuti asalowe dzikoli Yehova adawapatsa.