Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:7 - Buku Lopatulika

Pomemeza msonkhano mulize, wosati chokweza ai.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pomemeza msonkhano mulize, wosati chokweza ai.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene mpingo wonse uyenera kusonkhana pamodzi, mulize lipenga, koma musalize lipenga lochenjeza.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pofuna kusonkhanitsa anthu, muziliza malipenga, koma mosiyana ndi mmene malipenga ochenjeza amalizidwira.

Onani mutuwo



Numeri 10:7
3 Mawu Ofanana  

Muombe lipenga mu Ziyoni, nimufuulitse m'phiri langa lopatulika; onse okhala m'dziko anjenjemere; pakuti tsiku la Yehova lilinkudza, pakuti liyandikira;


Ana aamuna a Aroni, ansembe, ndiwo aziliza malipenga; ndipo akhale kwa inu lemba losatha ku mibadwo yanu.