Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:36 - Buku Lopatulika

Ndi pakupumula ili anati, Bwerani Yehova kwa zikwizikwi za Israele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi pakupumula ili anati, Bwerani Yehova kwa zikwizikwi za Israele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtambowo ukaima, Mose ankati, “Inu Chauta, bwererani kwa Aisraele anu amene ali zikwi zosaŵerengeka.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Pamene likupumula, ankanena kuti, “Bwererani, Inu Yehova, ku chinamtindi cha Aisraeli.”

Onani mutuwo



Numeri 10:36
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anamdalitsa Rebeka, nati kwa iye, Mlongo wathu ndiwe, iwe ukhale amai wa anthu zikwizikwi, mbeu zako zigonjetse chipata cha iwo akudana nao.


Ukani, Yehova, lowani ku mpumulo wanu; Inu ndi hema wa mphamvu yanu.


Yehova bwanji mwatisocheretsa kusiya njira zanu, ndi kuumitsa mitima yathu tisakuopeni? Bwerani, chifukwa cha atumiki anu, mafuko a cholowa chanu.


Yehova Mulungu wanu anakuchulukitsani, ndipo taonani, lero muchuluka ngati nyenyezi za kumwamba.