Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:31 - Buku Lopatulika

Koma anati, Usatisiyetu; popeza udziwa poyenera kumanga ife m'chipululu, ndipo udzakhala maso athu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma anati, Usatisiyetu; popeza udziwa poyenera kumanga ife m'chipululu, ndipo udzakhala maso athu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndipo Mose adati, “Musatisiye, ndapota nanu, poti inu mukudziŵa kumene tingamange mahema m'chipululu muno, ndipo mudzakhala maso athu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Mose anati, “Pepa usatisiye popeza ukudziwa kumene tingamange misasa mʼchipululu muno ndipo udzakhala maso athu.

Onani mutuwo



Numeri 10:31
5 Mawu Ofanana  

Ndinali maso a akhungu, ndi mapazi a otsimphina.


Ine ndidzakulangiza ndi kuphunzitsa iwe za njira ukayendayo; ndidzakupangira ndi diso langa lakuyang'ana iwe.


Ndipo kudzatero, ukamuka nafe, inde, kudzali kuti zokoma zilizonse Yehova atichitira ife, zomwezo tidzakuchitira iwe.


Nyamuliranani zothodwetsa, ndipo kotero mufitse chilamulo cha Khristu.