Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Numeri 10:27 - Buku Lopatulika

Ndi pa gulu la fuko la ana a Nafutali anayang'anira Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi pa gulu la fuko la ana a Nafutali anayang'anira Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mtsogoleri wa gulu la fuko la Nafutali anali Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndipo mtsogoleri wa mtundu wa Nafutali anali Ahira mwana wa Enani.

Onani mutuwo



Numeri 10:27
4 Mawu Ofanana  

Wa Nafutali, Ahira mwana wa Enani.


Ndi pa gulu la fuko la ana a Asere anayang'anira Pagiyele mwana wa Okarani.


Potero maulendo a ana a Israele anakhala monga mwa magulu ao; nayenda ulendo wao.


Tsiku lakhumi ndi chiwiri kalonga wa ana a Nafutali, ndiye Ahira mwana wa Enani: